Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 20:37 - Buku Lopatulika

37 Ndipo mnyamatayo atafika pamalo a muvi umene Yonatani anauponya, Yonatani anafuulira mnyamatayo, nati, Muviwo suli m'tsogolo mwako kodi?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

37 Ndipo mnyamatayo atafika pa malo a muvi umene Yonatani anauponya, nati, Muviwo suli m'tsogolo mwako kodi?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

37 Ndipo mnyamatayo atafika pamalo pomwe padaagwa muviwo, Yonatani adanena chokweza kuti, “Muvi uli patsogolo pakopo.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

37 Mnyamatayo atafika pamene muvi wa Yonatani unagwera,

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 20:37
2 Mawu Ofanana  

Koma ndikati kwa mnyamatayo, Ona mivi ili kutsogoloko; pamenepo unyamuke ulendo wako; popeza Yehova wakuuza umuke.


Ndipo Yonatani anafuulira mnyamatayo, nati, Yendetsa, fulumira, usaima. Ndi mnyamata wa Yonatani anatola mivi, nafika kwa mbuye wake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa