1 Samueli 20:32 - Buku Lopatulika32 Ndipo Yonatani anayankha Saulo atate wake, nanena, Aphedwe chifukwa ninji? Anachitanji? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Ndipo Yonatani anayankha Saulo atate wake, nanena, Aphedwe chifukwa ninji? Anachitanji? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Yonatani adafunsa bambo wake kuti, “Kodi chifukwa chiyani mufuna kumupha Davide? Kodi walakwa chiyani?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Yonatani anafunsa abambo ake kuti, “Nʼchifukwa chiyani mufuna kuti Davide aphedwe? Iye walakwa chiyani?” Onani mutuwo |