1 Samueli 20:31 - Buku Lopatulika31 Popeza nthawi yonse mwana wa Yeseyo akhala ndi moyo padziko, koma sudzakhazikika iwe, kapena ufumu wako. Chifukwa chake tumiza tsopano numtengere kuno kwa ine, popeza adzafa ndithu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Popeza nthawi yonse mwana wa Yeseyo akhala ndi moyo padziko, koma sudzakhazikika iwe, kapena ufumu wako. Chifukwa chake tumiza tsopano numtengere kuno kwa ine, popeza adzafa ndithu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Kodi sukudziŵa kuti mwana wa Yese akakhalabe ndi moyo pa dziko lapansi, iweyo sudzakhala mfumu? Nchifukwa chake tsono, tuma anthu kuti akamtenge, abwere naye kuno, pakuti ndithudi adzafa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Mwana wa Yese akakhala ndi moyo pa dziko lapansi lino, iwe sudzakhala mfumu. Tsopano tumiza munthu akamutenge kubwera naye kwa ine, pakuti Davide ayenera kufa basi!” Onani mutuwo |