Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 20:33 - Buku Lopatulika

33 Ndipo Saulo anamponyera mkondo kuti amgwaze; momwemo Yonatani anazindikira kuti atate wake anatsimikiza mtima kupha Davide.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

33 Ndipo Saulo anamponyera mkondo kuti amgwaze; momwemo Yonatani anazindikira kuti atate wake anatsimikiza mtima kupha Davide.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

33 Atamva zimenezi Saulo adamponyera mkondo Yonataniyo kuti amuphe. Pamenepo Yonatani adadziŵa kuti bambo wake watsimikizadi mtima kuti aphe Davide.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

33 Apo Sauli anamuponyera mkondo wake kuti amuphe. Tsono Yonatani anadziwa kuti abambo ake atsimikiza mtima kuti aphe Davide.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 20:33
5 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake Solomoni anafuna kupha Yerobowamu, ndipo Yerobowamu anathawira ku Ejipito kwa Sisake mfumu ya Aejipito, nakhala mu Ejipito kufikira imfa ya Solomoni.


Ndipo Saulo anaponya mkondowo; pakuti anati, Ndidzapyoza Davide ndi kumphatikiza ndi khoma. Ndipo Davide analewa kawiri kuchoka pamaso pake.


Ndipo Saulo anayesa kupyoza Davide kumphatikiza kukhoma ndi mkondowo; koma iye anadzilanditsa kuchoka pamaso pa Saulo; ndipo analasa khoma; ndipo Davide anathawa napulumuka usiku uja.


Pamenepo Yonatani anauka pagome wolunda ndithu, osadya kanthu tsiku lachiwiri la mwezi, pakuti mtima wake unali ndi chisoni chifukwa cha Davide, popeza atate wake anamchititsa manyazi.


Tsono akati, Chabwino; kapolo wako adzakhala ndi mtendere; koma akapsa mtima, uzindikirepo kuti anatsimikiza mtima kundichitira choipa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa