1 Samueli 20:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo Davide analumbiranso nati, Atate wako adziwatu kuti wandikomera mtima; nati, Yonatani asadziwe ichi, kuti angamve chisoni; koma pali Yehova, ndiponso pali moyo wako, pakati pa ine ndi imfa pali ngati phazi limodzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo Davide analumbiranso nati, Atate wako adziwatu kuti wandikomera mtima; nati, Yonatani asadziwe ichi, kuti angamve chisoni; koma pali Yehova, ndiponso pali moyo wako, pakati pa ine ndi imfa pali ngati phazi limodzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Koma Davide adalumbira kuti, “Abambo ako akudziŵa bwino lomwe kuti umandikonda, ndipo adati, ‘Yonatani asadziŵe zimenezi kuwopa kuti angamve chisoni.’ Koma ndithu, Mulungudi, iwe Yonatani uli apa, imfa sili nane kutali.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Koma Davide analumbira kuti, “Abambo ako akudziwa bwino lomwe kuti iwe umandikonda ndipo iwo amaganiza kuti, Yonatani sayenera kudziwa zimenezi mwina adzamva chisoni kwambiri. Komabe, pali Yehova ndi pali iwe, imfa sinanditalikire.” Onani mutuwo |