1 Samueli 20:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo Yonatani anamlumbiritsa Davide kachiwiri, chifukwa anamkonda; popeza anamkonda monga anakonda moyo wa iye yekha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo Yonatani anamlumbiritsa Davide kachiwiri, chifukwa anamkonda; popeza anamkonda monga anakonda moyo wa iye yekha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Apo Yonatani adalumbiritsanso Davide kuti asaleke kumkonda, pakuti Yonatani ankakonda Davide monga momwe ankadzikondera iye mwini. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Kenaka Yonatani anamulumbiritsanso Davide kuti asaleke kumukonda, pakuti ankamukonda monga ankadzikondera yekha. Onani mutuwo |