1 Samueli 20:16 - Buku Lopatulika16 Chomwecho Yonatani anapangana pangano ndi nyumba ya Davide, ndipo Yehova anakwaniritsa izi polanga adani a Davide. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Chomwecho Yonatani anapangana pangano ndi nyumba ya Davide, ndipo Yehova anakwaniritsa izi polanga adani a Davide. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 banja la ine Yonatani lisadzafafanizike nao. Ndithu Chauta alipsire pa adani ake a Davide.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 “Dzina la ine Yonatani lisadzafafanizidwe nawo pamodzi. Yehova alange adani onse a Davide.” Onani mutuwo |