1 Samueli 20:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo undionetsere chifundo cha Yehova, si pokhala ine ndi moyo pokha, kuti ndingafe; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo undionetsere chifundo cha Yehova, si pokhala ine ndi moyo pokha, kuti ndingafe; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Ndikakhala ndili moyobe, udzandiwonetse kukoma mtima konga kwa Chauta. Koma ndikafa, usadzaleke kuchitira chifundo banja langa mpaka muyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Ndikakhalabe ndi moyo udzandionetse kukoma mtima monga kwa Yehova nthawi yonse ya moyo wanga, kuti ine ndisaphedwe. Onani mutuwo |