1 Samueli 2:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo zoipa za anyamatawo zinali zazikulu ndithu pamaso pa Yehova; pakuti anthu anaipidwa ndi nsembe ya Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo zoipa za anyamatawo zinali zazikulu ndithu pamaso pa Yehova; pakuti anthu anaipidwa ndi nsembe ya Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Motero tchimo la ana a Eli linali lalikulu pamaso pa Chauta, pakuti ankanyoza nsembe za Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Tchimo la ana a Eli linali lalikulu kwambiri pamaso pa Yehova pakuti iwo amanyoza nsembe za Yehova. Onani mutuwo |