1 Samueli 2:18 - Buku Lopatulika18 Koma Samuele anatumikira pamaso pa Yehova akali mwana, atamangira m'chuuno ndi efodi wabafuta. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Koma Samuele anatumikira pamaso pa Yehova akali mwana, atamangira m'chuuno ndi efodi wabafuta. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Samuele pa unyamata wake ankatumikira pamaso pa Chauta, atavala efodi yabafuta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Koma Samueli amatumikira pamaso pa Yehova atavala efodi ya nsalu yofewa yosalala. Onani mutuwo |