1 Samueli 19:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo pamene anauza Saulo, iye anatumiza mithenga ina; koma iyonso inanenera. Ndipo Saulo anatumiza mithenga kachitatu, nayonso inanenera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo pamene anauza Saulo, iye anatumiza mithenga ina; koma iyonso inanenera. Ndipo Saulo anatumiza mithenga kachitatu, nayonso inanenera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Saulo atazimva zimenezo, adatuma anthu ena, ndipo nawonso adayamba kulosa. Adatumanso anthu ena kachitatu, nawonso adayamba kulosa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Sauli atamva zimenezi anatumizanso anthu ena, koma nawonso anayamba kulosa. Anatumanso anthu ena kachitatu, koma nawonso anayamba kulosa. Onani mutuwo |