Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 19:12 - Buku Lopatulika

12 Chomwecho Mikala anamtsitsira Davide pazenera, namuka iye, nathawa, napulumuka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Chomwecho Mikala anamtsitsira Davide pazenera, namuka iye, nathawa, napulumuka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Choncho Mikala adamtulutsira Davideyo pa windo, ndipo adathaŵa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Choncho Mikala anamutulutsira Davide pa zenera, ndipo anathawa ndi kupulumuka.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 19:12
6 Mawu Ofanana  

Ndipo anyamata a Abisalomu anafika kunyumba kwa mkaziyo; nati, Ali kuti Ahimaazi ndi Yonatani? Ndipo mkaziyo ananena nao, Anaoloka kamtsinje kamadzi. Ndipo atawafunafuna, osawapeza, anabwerera kunka ku Yerusalemu.


Masautso a wolungama mtima achuluka, koma Yehova amlanditsa mwa onsewa.


Pamenepo anawatsitsa pazenera ndi chingwe; popeza nyumba yake inali pa linga la mzinda, nakhala iye palingapo.


Ndipo ana a Saulo ndiwo Yonatani, ndi Isivi, ndi Malikisuwa; ndi maina a ana aakazi ake awiri ndi awa: dzina la woyamba ndiye Merabi, ndi dzina la mng'ono wake ndiye Mikala;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa