1 Samueli 19:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo Saulo anayesa kupyoza Davide kumphatikiza kukhoma ndi mkondowo; koma iye anadzilanditsa kuchoka pamaso pa Saulo; ndipo analasa khoma; ndipo Davide anathawa napulumuka usiku uja. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo Saulo anayesa kupyoza Davide kumphatikiza kukhoma ndi mkondowo; koma iye anadzilanditsa kuchoka pamaso pa Saulo; ndipo analasa khoma; ndipo Davide anathawa napulumuka usiku uja. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Pomwepo Saulo adayesa kubaya Davide ndi kumkhomera ku chipupa. Koma Davide adauleŵa mkondowo, kotero kuti udangolasa chipupa. Ndipo adathaŵa napulumuka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Sauli anafuna kumubaya Davide ndi kumukhomera kukhoma, koma Davide anapewa mkondowo kotero Sauli anakabaya pa khoma. Usiku womwewo Davide anathawa. Onani mutuwo |