1 Samueli 18:30 - Buku Lopatulika30 Pomwepo mafumu a Afilisti anatuluka; ndipo nthawi zonse anatuluka iwo, Davide anali wochenjera koposa anyamata onse a Saulo, chomwecho dzina lake linatamidwa kwambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Pomwepo mafumu a Afilisti anatuluka; ndipo nthawi zonse anatuluka iwo, Davide anali wochenjera koposa anyamata onse a Saulo, chomwecho dzina lake linatamidwa kwambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Tsono pamene Afilisti ankatuluka kukamenya nkhondo, nthaŵi zonse Davide ankapambana kwambiri kuposa atsogoleri ena onse a ankhondo a Saulo. Choncho dzina lake la Davide lidatchuka kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Nthawi zonse pamene atsogoleri a Afilisti ankatuluka kukamenya nkhondo, Davide ankapambana kuposa nduna zonse za Sauli. Choncho dzina lake linatchuka kwambiri. Onani mutuwo |