1 Samueli 18:29 - Buku Lopatulika29 Saulo nayamba kumuopa Davide kopambana; ndi Saulo anali mdani wa Davide masiku onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Saulo nayamba kumuopa Davide kopambana; ndi Saulo anali mdani wa Davide masiku onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 adamuwopabe kwambiri ndi kudana naye moyo wake wonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 iye anapitirirabe kumuopa Davide ndi kumadana naye moyo wake wonse. Onani mutuwo |