Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 18:26 - Buku Lopatulika

26 Ndipo pamene anyamata ake anauza Davide mau awa, kudamkomera Davide kukhala mkamwini wa mfumu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Ndipo pamene anyamata ake anauza Davide mau awa, kudamkomera Davide kukhala mkamwini wa mfumu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 Ndiye nduna za Saulozo zitamuuza Davide mau ameneŵa, zidamkondweretsa kuti akhale mkamwini wa mfumu. Nthaŵi yoti atenge mkazi wake isanakwane,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 Nduna za Saulizo zitamuwuza Davide zimenezi, anakondwera kuti akhale mpongozi wa mfumu. Koma nthawi imene anapatsidwa isanathe,

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 18:26
2 Mawu Ofanana  

Ndipo anthu aja anati kwa Loti, Kodi muli nao ena pano? Mkamwini, ndi ana ako aamuna, ndi ana ako aakazi, ndi onse ali nao m'mzinda muno, utuluke nao m'malo muno:


Nati Saulo, Ndidzampatsa iye, kuti amkhalire msampha, ndi kuti dzanja la Afilisti limgwere. Chifukwa chake Saulo ananena ndi Davide, Lero udzakhala mkamwini wanga kachiwiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa