Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 18:24 - Buku Lopatulika

24 Ndipo anyamata a Saulo anamuuza, kuti, Anatero Davide.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Ndipo anyamata a Saulo anamuuza, kuti, Anatero Davide.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Nduna za Saulo zidamuuza zonse zimene Davide adaanena.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Nduna za Sauli zinamuwuza zonse zimene anayankha Davide.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 18:24
2 Mawu Ofanana  

Ndipo anyamata a Saulo analankhula mau awa m'makutu a Davide. Nati Davide, Kodi muchiyesera chinthu chopepuka kukhala mkamwini wa mfumu, popeza ndili munthu wosauka, ndi wopeputsidwa.


Nati Saulo, Mudzatero kwa Davide, kuti mfumu safuna cholowolera china, koma nsonga za makungu zana limodzi za Afilisti, kuti abwezere chilango adani a mfumu. Koma Saulo anaganizira kupha Davide ndi dzanja la Afilisti.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa