1 Samueli 18:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo pamene Saulo anaona kuti analikukhala wochenjera ndithu anamuopa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo pamene Saulo anaona kuti analikukhala wochenjera ndithu anamuopa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Tsono pamene Saulo adaona kuti Davide akupambana kwambiri, adayamba kuchita naye mantha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Sauli ataona momwe Davide ankapambanira, iye anamuopa kwambiri. Onani mutuwo |