1 Samueli 18:16 - Buku Lopatulika16 Koma Aisraele onse ndi Ayuda onse anamkonda Davide pakuti anawatsogolera kutuluka ndi kulowa nao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Koma Aisraele onse ndi Ayuda onse anamkonda Davide pakuti anawatsogolera kutuluka ndi kulowa nao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Koma anthu onse a ku Israele ndi a ku Yuda ankamkonda Davide, chifukwa iyeyu ankaŵatsogolera namapambana pa zonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Koma Aisraeli onse ndi anthu a Yuda ankamukonda Davide chifukwa ankawatsogolera pa nkhondo zawo. Onani mutuwo |