Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 17:57 - Buku Lopatulika

57 Ndipo pamene Davide anabwera, atapha Mfilistiyo, Abinere anamtenga, nafika naye pamaso pa Saulo, mutu wa Mfilistiyo uli m'dzanja lake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

57 Ndipo pamene Davide anabwera, atapha Mfilistiyo, Abinere anamtenga, nafika naye pamaso pa Saulo, mutu wa Mfilistiyo uli m'dzanja lake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

57 Tsono pamene Davide ankabwererako kumene adaakapha Mfilisti kuja, Abinere adamtenga napita naye kwa Saulo, mutu wa Mfilisti uja uli m'manja mwake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

57 Davide atangobwerako kokapha Mfilisiti kuja, Abineri anamutenga nabwera naye kwa Sauli, mutu wa Mfilisiti uja uli mʼmanja mwake.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 17:57
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Davide anatenga mutu wa Mfilistiyo, napita nao ku Yerusalemu; koma zida zake anazisunga m'hema wake.


Ndipo mfumu inati, Ufunsire kuti mnyamatayo ndi mwana wa yani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa