1 Samueli 17:56 - Buku Lopatulika56 Ndipo mfumu inati, Ufunsire kuti mnyamatayo ndi mwana wa yani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201456 Ndipo mfumu inati, Ufunsire kuti mnyamatayo ndi mwana wa yani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa56 Apo mfumu idati, “Kafunse kuti kodi mnyamata ameneyu ndi mwana wa yani?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero56 Mfumu inati, “Pita kafufuze kuti mnyamata ameneyu ndi mwana wa yani.” Onani mutuwo |