1 Samueli 17:50 - Buku Lopatulika50 Chomwecho Davide anapambana Mfilistiyo ndi mwala wa choponyera chake, nakantha Mfilistiyo, namupha. Koma m'dzanja la Davide munalibe lupanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201450 Chomwecho Davide anapambana Mfilistiyo ndi mwala wa choponyera chake, nakantha Mfilistiyo, namupha. Koma m'dzanja la Davide munalibe lupanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa50 Choncho Davide adampambana Goliyati uja pomlasa ndi mwala wam'khwenengwe, namupha Mfilistiyo. M'manja mwa Davide munalibe konse lupanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero50 Kotero Davide anamupambana Mfilisitiyo pomugenda ndi mwala wa legeni ndi kumupha. Mʼmanja mwa Davide munalibe lupanga. Onani mutuwo |