1 Samueli 17:43 - Buku Lopatulika43 Ndipo Mfilisti anati kwa Davide, Ine ndine galu kodi, kuti iwe ukudza kwa ine ndi ndodo? Ndi Mfilistiyo anatukwana Davide natchula milungu yake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201443 Ndipo Mfilisti anati kwa Davide, Ine ndine galu kodi, kuti iwe ukudza kwa ine ndi ndodo? Ndi Mfilistiyo anatukwana Davide natchula milungu yake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa43 Tsono adafunsa Davide kuti, “Kodi ndine galu, kuti uzibwera kwa ine ndi ndodo?” Pompo adayamba kutemberera Davide potchula milungu yake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero43 Iye anati kwa Davide, “Kodi ndine galu, kuti ubwere kwa ine ndi ndodo?” Ndipo Mfilisitiyo anamutemberera Davide potchula mayina a milungu yake. Onani mutuwo |