1 Samueli 17:41 - Buku Lopatulika41 Ndipo Mfilistiyo anadza, nayandikira kwa Davide; ndi wonyamula chikopa chake anamtsogolera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Ndipo Mfilistiyo anadza, nayandikira kwa Davide; ndi wonyamula chikopa chake anamtsogolera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Tsono Mfilistiyo adayambapo kupita kumene kunali Davide, munthu wonyamula chishango ali patsogolo pake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Tsono Mfilisiti uja anayambapo kupita kumene kunali Davide, mnyamata wonyamula zida zake za nkhondo ali patsogolo pake. Onani mutuwo |