Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 17:30 - Buku Lopatulika

30 Napotolokera iye kwa munthu wina, nalankhula mau omwewo; ndipo anthu anamyankhanso monga momwemo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Napotolokera iye kwa munthu wina, nalankhula mau omwewo; ndipo anthu anamyankhanso monga momwemo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Tsono adachoka apo napita kwa wina namufunsa zokhazokhazo. Aliyense adamuyankhanso monga poyamba paja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Ndipo anamuchokera napita kwa munthu wina ndipo anamufunsa nkhani yomweyo, ndipo anthu anamuyankha iye monga poyamba paja.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 17:30
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Davide anati, Ndachitanji tsopano? Palibe chifukwa kodi?


Ndipo pamene mau adanena Davide anamveka, anawapitiriza kwa Saulo; ndipo iye anamuitana.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa