1 Samueli 17:29 - Buku Lopatulika29 Ndipo Davide anati, Ndachitanji tsopano? Palibe chifukwa kodi? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Ndipo Davide anati, Ndachitanji tsopano? Palibe chifukwa kodi? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Davide adati, “Kodi ndachimwa chiyani? Ndiye kuti ndileke nkulankhula komwe?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Davide anati, “Kodi ndachita chiyani ine? Kodi ndisamayankhule?” Onani mutuwo |