Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 17:29 - Buku Lopatulika

29 Ndipo Davide anati, Ndachitanji tsopano? Palibe chifukwa kodi?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 Ndipo Davide anati, Ndachitanji tsopano? Palibe chifukwa kodi?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 Davide adati, “Kodi ndachimwa chiyani? Ndiye kuti ndileke nkulankhula komwe?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 Davide anati, “Kodi ndachita chiyani ine? Kodi ndisamayankhule?”

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 17:29
6 Mawu Ofanana  

Mayankhidwe ofatsa abweza mkwiyo; koma mau owawitsa aputa msunamo.


Koma iye amene ali wauzimu ayesa zonse, koma iye yekha sayesedwa ndi mmodzi yense.


osabwezera choipa ndi choipa, kapena chipongwe ndi chipongwe, koma penatu madalitso; pakuti kudzatsata ichi mwaitanidwa, kuti mukalandire dalitso.


Ndipo Eliabu mkulu wake anamumva iye alikulankhula ndi anthu; ndipo Eliyabu anapsa mtima ndi Davide, nati, Unatsikiranji kuno? Ndi nkhosa zija zowerengeka unazisiya ndi yani, m'chipululu muja? Ine ndidziwa kudzikuza kwako ndi kuipa kwa mtima wako; pakuti watsika kuti udzaone nkhondoyi.


Napotolokera iye kwa munthu wina, nalankhula mau omwewo; ndipo anthu anamyankhanso monga momwemo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa