Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 16:8 - Buku Lopatulika

8 Pamenepo Yese anaitana Abinadabu nampititsa pa Samuele. Ndipo iye adati, Koma uyunso Yehova sadamsankhe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Pamenepo Yese anaitana Abinadabu nampititsa pa Samuele. Ndipo iye adati, Koma uyunso Yehova sadamsankhe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Tsono Yese adaitana Abinadabu namtumiza kwa Samuele. Ndipo Samuele adati, “Ameneyunso Chauta sadamsankhe.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Kenaka Yese anayitana Abinadabu namubweretsa pamaso pa Samueli. Koma Samueli anati, “Yehova sanamusankhenso ameneyu.”

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 16:8
4 Mawu Ofanana  

Benabinadabu ku mtunda wa Dori, mkazi wake ndiye Tafati mwana wa Solomoni;


ndi Yese anabala mwana wake wamwamuna woyamba Eliyabu, ndi Abinadabu wachiwiri, ndi Simea wachitatu,


Ndipo ana atatu aakulu a Yese anatsata Saulo kunkhondoko; ndi maina ao a ana ake atatuwo adapita ku nkhondowo ndiwo Eliyabu woyambayo, ndi mnzake womponda pamutu pake Abinadabu, ndi wachitatu Sama.


Ndipo anthu a ku Kiriyati-Yearimu anabwera, natenga likasa la Yehova, nafika nalo m'nyumba ya Abinadabu paphiri; napatula mwana wake wamwamuna Eleazara kuti asunge likasa la Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa