1 Samueli 16:5 - Buku Lopatulika5 Nati iye, Ndi mtendere umene; ndadza kudzaphera nsembe kwa Yehova; mudzipatule ndi kufika ndi ine kunsembeko. Ndipo iye anapatula Yese ndi ana ake, nawaitanira kunsembeko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Nati iye, Ndi mtendere umene; ndadza kudzaphera nsembe kwa Yehova; mudzipatule ndi kufika ndi ine kunsembeko. Ndipo iye anapatula Yese ndi ana ake, nawaitanira kunsembeko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Samuele adayankha kuti, “Inde, nkwabwino. Ndadzapereka nsembe kwa Chauta. Mudzipatule, ndipo mupite nane kukapereka nsembe.” Pamenepo Samuele adapatula Yese ndi ana ake aamuna, ndipo adaŵaitana kuti akapereke nao nsembe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Samueli anayankha kuti, “Inde, kwabwino. Ndabwera kudzapereka nsembe kwa Yehova. Mudzipatule ndipo mubwere kudzapereka nsembe pamodzi nane.” Kenaka iye anamupatula Yese ndi ana ake aamuna ndipo anawayitana kudzapereka nsembe. Onani mutuwo |