Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 16:23 - Buku Lopatulika

23 Ndipo kunali kuti pamene mzimu woipawo wochokera kwa Mulungu unali pa Saulo, Davide anatenga zeze, naliza ndi dzanja lake; chomwecho Saulo anatsitsimuka, nakhala bwino, ndi mzimu woipa unamchokera iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndipo kunali kuti pamene mzimu woipawo wochokera kwa Mulungu unali pa Saulo, Davide anatenga zeze, naliza ndi dzanja lake; chomwecho Saulo anatsitsimuka, nakhala bwino, ndi mzimu woipa unamchokera iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Tsono nthaŵi zonse mzimu woipa uja ukamfikira Saulo, Davide ankatenga zeze namamuimba. Motero Saulo ankapeza bwino, ndipo mzimu woipawo unkamsiya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Nthawi zonse mzimu woyipa wochokera kwa Mulungu umati ukamufikira Sauli, Davide ankatenga zeze wake nʼkumamuyimbira. Choncho Sauli ankapeza bwino, ndipo mzimu woyipa uja unkamusiya.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 16:23
6 Mawu Ofanana  

Koma tsopano, nditengereni wanthetemya. Ndipo kunali, wanthetemyayo ali chiimbire, dzanja la Yehova linamgwera.


Ndipo Saulo anatumiza kwa Yese, nati, Ulole kuti Davide aime pamaso panga; pakuti ndamkomera mtima.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa