1 Samueli 16:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo Davide anafika kwa Saulo, naima pamaso pake; ndipo iye anamkonda kwambiri, namsandutsa wonyamula zida zake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo Davide anafika kwa Saulo, naima pamaso pake; ndipo iye anamkonda kwambiri, namsandutsa wonyamula zida zake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Motero Davide adafika kwa Saulo, nayamba ntchito yake yomtumikira. Saulo adamkonda kwambiri, namsandutsa wonyamula zida zake zankhondo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Davide anafika kwa Sauli ndipo anayamba ntchito. Sauli anamukonda kwambiri Davide ndipo anamusandutsa wonyamula zida zake za nkhondo. Onani mutuwo |