1 Samueli 16:19 - Buku Lopatulika19 Chifukwa chake Saulo anatumiza mithenga kwa Yese, nati, Unditumizire Davide, mwana wako, amene ali kunkhosa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Chifukwa chake Saulo anatumiza mithenga kwa Yese, nati, Unditumizire Davide, mwana wako, amene ali kunkhosa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Choncho Saulo adatuma amithenga kwa Yese kukanena kuti, “Tumizire Davide mwana wako, uja amaŵeta nkhosayu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Ndipo Sauli anatumiza amithenga kwa Yese kukanena kuti, “Nditumizireni mwana wanu Davide, amene amaweta nkhosa.” Onani mutuwo |