1 Samueli 16:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo Saulo anati kwa anyamata ake, Mundifunire tsono munthu wakudziwa kuimba bwino, nimubwere naye kwa ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo Saulo anati kwa anyamata ake, Mundifunire tsono munthu wakudziwa kuimba bwino, nimubwere naye kwa ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Pamenepo Saulo adaŵauza kuti, “Chabwino mundifunire munthu wodziŵa bwino kuimba kwake, ndipo mubwere naye kuno.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Choncho Sauli anati kwa atumiki ake, “Chabwino, kandipezereni munthu wodziwa bwino kuyimba ndipo mubwere naye kuno.” Onani mutuwo |