1 Samueli 16:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo anyamata a Saulo ananena naye, Onani tsopano, mzimu woipa wochokera kwa Mulungu ulikuvuta inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo anyamata a Saulo ananena naye, Onani tsopano, mzimu woipa wochokera kwa Mulungu ulikuvuta inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Atumiki ake adamuuza kuti, “Onani, tsopano mzimu woipa, wotumidwa ndi Mulungu, ukukuzunzani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Atumiki a Sauli anati, “Taonani mzimu woyipa wochokera kwa Mulungu ukukuzunzani. Onani mutuwo |