Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 15:18 - Buku Lopatulika

18 Ndipo Yehova anakutumani ulendo, kuti, Muka, nuononge konsekonse Aamaleke akuchita zoipawo, nuponyane nao kufikira utawatha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndipo Yehova anakutumani ulendo, kuti, Muka, nuononge konsekonse Aamaleke akuchita zoipawo, nuponyane nao kufikira utawatha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Ndipo Chauta adakutumani kuti, ‘Pita, ukaononge kwathunthu Aamaleke, anthu oipa mtima aja, ndipo uchite nawo nkhondo mpaka kuŵatheratu onsewo.’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Ndipo Yehova anakutumani kuti, ‘Pitani mukawononge kwathunthu Aamaleki, anthu oyipa aja. Mukachite nawo nkhondo mpaka kuwatheratu.’

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 15:18
9 Mawu Ofanana  

Ndipo anthu a ku Sodomu anali oipa ndi ochimwa kwambiri pamaso pa Yehova.


Ndipo anabwera nafika ku Enimisipati (kumeneko ndi ku Kadesi), nakantha dziko lonse la Aamaleke, ndiponso Aamori amene akhala mu Hazazoni-Tamara.


Koma iwo adzabweranso kuno mbadwo wachinai: pakuti mphulupulu za Aamori sizinakwaniridwe.


Si ndizo chionongeko cha wosalungama, ndi tsoka la ochita mphulupulu?


Njira ya Yehova ndi linga kwa woongoka mtima; koma akuchita zoipa adzaonongeka.


Zoipa zilondola ochimwa; koma olungama adzalandira mphotho yabwino.


mbale zofukizazo za iwo amene adachimwira moyo waowao, ndipo azisule zaphanthiphanthi, zikhale chivundikiro cha guwa la nsembe; popeza anabwera nazo pamaso pa Yehova, chifukwa chake zikhala zopatulika; ndipo zidzakhala chizindikiro kwa ana a Israele.


Ife ndife Ayuda pachibadwidwe, ndipo sitili ochimwa a kwa amitundu;


Muka tsopano, nukanthe Amaleke, nuononge konsekonse zonse ali nazo, usawalekerere, koma uwaphe mwamuna ndi mkazi, mwana ndi woyamwa, ng'ombe ndi nkhosa, ngamira ndi bulu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa