Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 14:9 - Buku Lopatulika

9 Akatero ndi ife kuti, Baimani kufikira titsikira kwa inu; tsono tidzaima m'malo mwathu, osakwera kwa iwo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Akatero ndi ife kuti, Baimani kufikira titsikira kwa inu; tsono tidzaima m'malo mwathu, osakwera kwa iwo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Akatiwuza kuti, ‘Dikirani mpaka tikupezeni,’ tikangoima pamalo pathu, osapita kwa iwowo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Akatiwuza kuti, ‘Imani pomwepo mpaka tikupezeni,’ ife tikangoyima pomwepo osapita kumene kuli iwoko.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 14:9
5 Mawu Ofanana  

nudzamva zonena iwo; utatero manja ako adzalimbikitsidwa kutsikira kumisasa. Pamenepo anatsikira ndi Pura mnyamata wake ku chilekezero cha anthu azida a m'misasa.


Koma akatero kuti, Kwerani kuno kwa ife, tsono tidzakwera; pakuti Yehova wawapereka m'manja mwathu; ndipo ichi chidzatikhalira chizindikiro.


Ndipo Yonatani anati, Taona, ife tidzapita kunka kwa anthuwo, ndipo tidzadziwulula kwa iwo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa