Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 14:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo Yonatani anati, Taona, ife tidzapita kunka kwa anthuwo, ndipo tidzadziwulula kwa iwo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo Yonatani anati, Taona, ife tidzapita kunka kwa anthuwo, ndipo tidzadziwulula kwa iwo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Tsono Yonatani adati, “Tiwolokere kwa anthuwo, ndipo tikadziwonetse kwa iwo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Yonatani anati, “Tiye tsono tiwoloke kupita kumene kuli anthuwo ndi kukadzionetsa kwa iwo.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 14:8
3 Mawu Ofanana  

Ndipo wonyamula zida zake anena naye, Chitani zonse zili mumtima mwanu; palukani, onani ndili pamodzi ndi inu monga mwa mtima wanu.


Akatero ndi ife kuti, Baimani kufikira titsikira kwa inu; tsono tidzaima m'malo mwathu, osakwera kwa iwo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa