1 Samueli 14:38 - Buku Lopatulika38 Ndipo Saulo anati, Musendere kuno, inu nonse akulu a anthu; kuti muzindikire ndi kuona m'mene muli choipa ichi lero. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 Ndipo Saulo anati, Musendere kuno, inu nonse akulu a anthu; kuti muzindikire ndi kuona m'mene muli choipa ichi lero. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 Apo Saulo adati, “Bwerani kuno nonse atsogoleri a anthu. Tiwone ndi tchimo lanji lachitika lero. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 Choncho Sauli anati, “Bwerani kuno nonse atsogoleri a anthu, ndipo tiyeni tione kuti kodi tchimo limeneli lachitika bwanji lero? Onani mutuwo |