Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 14:30 - Buku Lopatulika

30 Koposa kotani nanga, ngati anthu akadadya nakhuta zowawanya anazipeza za adani ao? Popeza tsopano palibe kuwapha kwakukulu kwa Afilisti.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Koposa kotani nanga, ngati anthu akadadya nakhuta zowawanya anazipeza za adani ao? Popeza tsopano palibe kuwapha kwakukulu kwa Afilisti.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Kukadakhala bwino kwambiri, anthu akadadya mwaufulu lero zofunkha zimene adazipeza kwa adani ao. Zidakatero bwenzi tsopano lino titapha Afilisti ambiri.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Zikanakhala zabwino kwambiri anthuwa akanadya lero zofunkha za adani awo. Zikanatero tikanapha Afilisti ochuluka.”

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 14:30
3 Mawu Ofanana  

Nzeru ipambana zida za nkhondo; koma wochimwa mmodzi aononga zabwino zambiri.


Ndipo Yonatani anati, Atate wanga wavuta dziko; onani m'maso mwanga mwayera, chifukwa ndinalawako pang'ono uchiwu.


Ndipo anakantha Afilisti tsiku lija kuyambira ku Mikimasi kufikira ku Ayaloni, ndipo anthu anafooka kwambiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa