1 Samueli 14:25 - Buku Lopatulika25 Ndipo anthu onsewo analowa munkhalango, panali uchi pansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndipo anthu onsewo analowa munkhalango, panali uchi pansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Tsono onse adaloŵa m'nkhalango ina m'mene munali uchi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Gulu lonse la ankhondo linalowa mʼnkhalango mmene munali uchi. Onani mutuwo |