1 Samueli 13:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo owawanya anatuluka ku zithando za Afilisti magulu atatu; gulu limodzi linalowa njira yonka ku Ofura, ku dera la Suwala; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo owawanya anatuluka ku zithando za Afilisti magulu atatu; gulu limodzi linalowa njira yonka ku Ofura, ku dera la Suwala; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Ankhondo a Filisti adatuluka kuchoka ku zithando zao m'magulu atatu. Gulu limodzi lidalunjika ku Ofura ku dziko la Suwala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Ankhondo a Afilisti anatuluka mʼmisasa yawo mʼmagulu atatu. Gulu lina linapita ku Ofiri ku dziko la Suwala. Onani mutuwo |