1 Samueli 13:18 - Buku Lopatulika18 gulu lina linalowa njira yonka ku Betehoroni; ndi gulu linanso linalowa ku njira ya kumalire, akuyang'ana ku chigwa cha Zeboimu kuchipululuko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 gulu lina linalowa njira yonka ku Betehoroni; ndi gulu linanso linalowa ku njira ya kumalire, akuyang'ana ku chigwa cha Zeboimu kuchipululuko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Gulu lina lidalunjika ku Betehoroni, ndipo lina lidalunjika ku malire oyang'anana ndi chigwa cha Zeboimu chakuchipululu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Gulu lina linalunjika ku Beti-Horoni, ndipo gulu lachitatu linalunjika ku malire oyangʼanana ndi chigwa cha Zeboimu cha ku chipululu. Onani mutuwo |