1 Samueli 12:25 - Buku Lopatulika25 Koma mukaumirirabe kuchita choipa, mudzaonongeka, inu ndi mfumu yanu yomwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Koma mukaumirirabe kuchita choipa, mudzaonongeka, inu ndi mfumu yanu yomwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Koma mukamachitabe zoipa, ndiye kuti inuyo pamodzi ndi mfumu yanu mudzaonongedwa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Komabe mukapitirira kuchita zoyipa, ndiye kuti inu pamodzi ndi mfumu yanu mudzachotsedwa.” Onani mutuwo |