1 Samueli 12:16 - Buku Lopatulika16 Chifukwa chake tsono, imani pano, muone chinthu ichi chachikulu Yehova adzachichita pamaso panu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Chifukwa chake tsono, imani pano, muone chinthu ichi chachikulu Yehova adzachichita pamaso panu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Nchifukwa chake tsono imani pomwepa, muwone chinthu chachikulu chimene Chauta akuchitireni mukupenya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 “Tsono imani pomwepa kuti muone chinthu chachikulu chimene Yehova ali pafupi kuchita pamaso panu! Onani mutuwo |