1 Samueli 12:15 - Buku Lopatulika15 Koma mukapanda kumvera mau a Yehova, ndi kupikisana ndi lamulo la Yehova, dzanja la Yehova lidzatsutsana nanu, monga linatsutsana ndi makolo anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Koma mukapanda kumvera mau a Yehova, ndi kupikisana ndi lamulo la Yehova, dzanja la Yehova lidzatsutsana nanu, monga linatsutsana ndi makolo anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Koma mukapanda kumvera mau a Chauta nkumakana malamulo ake, ndiye kuti Iye adzakulangani inu ndi mfumu yanu yomwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Koma mukapanda kumvera Yehova ndi kumupandukira, ndiye adzakulangani pamodzi ndi mfumu yanu yomwe. Onani mutuwo |