1 Samueli 12:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo pamene munaona kuti Nahasi mfumu ya ana a Amoni inadza kuponyana nanu, munanena ndi ine, Koma mfumu itiweruze; ngakhale mfumu yanu ndiye Yehova Mulungu wanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo pamene munaona kuti Nahasi mfumu ya ana a Amoni inadza kuponyana nanu, munanena ndi ine, Koma mfumu itiweruze; ngakhale mfumu yanu ndiye Yehova Mulungu wanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Tsono pamene mudaona kuti Nahasi, mfumu ya Aamoni, adadza kuti adzamenyane nane, mudandiwuza kuti, ‘Iyai, koma mfumu ndiyo imene idzatilamulire,’ chonsecho mfumu yanu inali Chauta, Mulungu wanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 “Koma mutaona kuti Nahasi mfumu ya Amoni inkabwera kudzamenyana nanu, inu munandiwuza kuti, ‘Ayi, ife tikufuna mfumu kuti itilamulire,’ ngakhale kuti Yehova Mulungu wanu ndiye anali mfumu yanu. Onani mutuwo |