1 Samueli 12:13 - Buku Lopatulika13 Chifukwa chake siyi mfumu imene munaisankha, imene munandipempha; ndipo taonani, Yehova anakuikirani mfumu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Chifukwa chake siyi mfumu imene munaisankha, imene munandipempha; ndipo taonani, Yehova anakuikirani mfumu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 “Tsopano nayi mfumu imene mudaisankha, imene mudachita kuipempha ija. Ndiyo imene Chauta wakupatsani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Tsopano nayi mfumu imene mwayisankha, imene munayipempha. Onani, Yehova wakupatsani mfumu. Onani mutuwo |