Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 11:12 - Buku Lopatulika

12 Ndipo anthu anati kwa Samuele, Ndani iye amene anati, Kodi Saulo adzatiweruza ife? Tengani anthuwo kuti tiwaphe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Ndipo anthu anati kwa Samuele, Ndani iye amene anati, Kodi Saulo adzatiweruza ife? Tengani anthuwo kuti tiwaphe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Apo anthu adamufunsa Samuele kuti, “Ndani amene ankanena kuti, ‘Kodi Saulo nkutilamulira ife?’ Bwera nawoni anthuwo kuti tiŵaphe.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Kenaka anthu anafunsa Samueli kuti, “Kodi ndani aja ankanena kuti, ‘Kodi Sauli nʼkutilamulira ife?’ Bwera nawoni kuno kuti tidzawaphe.”

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 11:12
3 Mawu Ofanana  

Dzanja lanu lidzapeza adani anu onse, dzanja lanu lamanja lidzapeza iwo akuda Inu.


Koma adani anga aja osafuna kuti ndidzakhala mfumu yao, bwerani nao kuno, nimuwaphe pamaso panga.


Koma oipa ena anati, Uyu adzatipulumutsa bwanji? Ndipo anampeputsa, osakampatsa mtulo. Koma iye anakhala chete.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa