1 Samueli 10:22 - Buku Lopatulika22 Chifukwa chake anaonjeza kufunsa Yehova, Watsala wina kodi woyenera kubwera kuno? Ndipo Yehova anati, Onani, alikubisala pakati pa akatundu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Chifukwa chake anaonjeza kufunsa Yehova, Watsala wina kodi woyenera kubwera kuno? Ndipo Yehova anati, Onani, alikubisala pakati pa akatundu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Tsono anthuwo adafunsa Chauta kuti, “Mwati munthuyo wafika kuno?” Chauta adayankha kuti, “Inde, akubisala pakati pa katundu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Tsono anthu anafunsanso kwa Yehova kuti, “Kodi munthuyu wabwera kale kuno?” Ndipo Yehova anayankha kuti, “Inde wabisala pakati pa katundu.” Onani mutuwo |