Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 10:14 - Buku Lopatulika

14 Ndipo mbale wa atate wake wa Saulo ananena kwa iye ndi mnyamata wake, Munanka kuti? Ndipo iye anati, Kukafuna abuluwo; ndipo pakuona kuti sitinawapeze, tinadza kwa Samuele.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Ndipo mbale wa atate wake wa Saulo ananena kwa iye ndi mnyamata wake, Munanka kuti? Ndipo iye anati, Kukafuna abuluwo; ndipo pakuona kuti sitinawapeza, tinadza kwa Samuele.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Mbale wa bambo wake wa Saulo ataona Sauloyo ndi mnyamata uja, adaŵafunsa kuti, “Mudaapita kuti?” Saulo adayankha kuti, “Tidaakafunafuna abulu. Titaona kuti sakupezeka, tidaapita kwa Samuele.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Tsono amalume ake a Sauli anamufunsa ndi mnyamata wake kuti, “Munapita kuti?” Iye anayakha, “Timakafunafuna abulu koma titaona kuti sakupezeka, tinapita kwa Samueli.”

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 10:14
5 Mawu Ofanana  

Pamenepo analowa, naima kwa mbuye wake. Ndipo Elisa ananena naye, Ufuma kuti Gehazi? Nati, Ngati mnyamata wanu wayenda konse?


Ndipo pamene adatha kunenera anafika kumsanjeko.


Ndipo mbale wa atate wa Saulo anati, Undiuze chimene Samuele analankhula nawe.


ndi dzina la mkazi wa Saulo ndi Ahinowamu mwana wa Ahimaazi; ndi dzina la kazembe wa khamu lankhondo lake ndiye Abinere mwana wa Nere, mbale wake wa atate wa Saulo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa