Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Samueli 10:13 - Buku Lopatulika

13 Ndipo pamene adatha kunenera anafika kumsanjeko.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndipo pamene adatha kunenera anafika kumsanjeko.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Atatha kulosako, Saulo adapita ku kachisi ku phiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Sauli atasiya kuloserako, anapita ku kachisi ku phiri.

Onani mutuwo Koperani




1 Samueli 10:13
2 Mawu Ofanana  

Ndipo munthu wina wa komweko anayankha nati, Ndipo atate wao ndiye yani? Chifukwa chake mauwa anakhala ngati mwambi, Kodi Saulonso ali mwa aneneri?


Ndipo mbale wa atate wake wa Saulo ananena kwa iye ndi mnyamata wake, Munanka kuti? Ndipo iye anati, Kukafuna abuluwo; ndipo pakuona kuti sitinawapeze, tinadza kwa Samuele.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa